Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 13:57
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 57 Choncho anayamba kukhumudwa naye.+ Koma Yesu anawauza kuti: “Mneneri salemekezedwa kwawo kapena mʼnyumba mwake, koma kwina.”+

  • Luka 4:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Iye ananena kuti: “Ndithu ndikukuuzani, palibe mneneri amene amalandiridwa kwawo.+

  • Yohane 4:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Yesu mwiniwakeyo anachitira umboni kuti mneneri salemekezedwa kwawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena