Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Aliyense amene amakonda kwambiri bambo ake kapena mayi ake kuposa ine ndi wosayenera kuti akhale wophunzira wanga. Komanso aliyense amene amakonda kwambiri mwana wake wamwamuna kapena wamkazi kuposa ine ndi wosayenera kuti akhale wophunzira wanga.+

  • Mateyu 19:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Aliyense amene wasiya nyumba, azichimwene, azichemwali, abambo, amayi, ana kapena minda chifukwa cha dzina langa adzalandira zochuluka kuwirikiza maulendo 100 kuposa zimenezi ndiponso adzapeza moyo wosatha.+

  • Luka 18:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Yesu anawauza kuti: “Ndithu ndikukuuzani, palibe amene wasiya nyumba, mkazi, azichimwene, makolo kapena ana, chifukwa cha Ufumu wa Mulungu+ 30 amene sadzapeza zochuluka kwambiri kuposa zimenezi mu nthawi ino, ndipo mu nthawi* imene ikubwerayo, adzapeza moyo wosatha.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena