Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 41:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ngakhale munthu amene ndinkakhala naye mwamtendere, amene ndinkamukhulupirira,+

      Munthu amene ankadya chakudya changa, watukula chidendene chake nʼkundiukira.+

  • Mateyu 26:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Akudya chakudyacho iye ananena kuti: “Ndithu ndikukuuzani, mmodzi wa inu andipereka.”+ 22 Chifukwa chomva chisoni kwambiri ndi zimenezi, aliyense anayamba kumufunsa kuti: “Ambuye, kodi ndine kapena?”

  • Luka 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma taonani! Wondipereka ndili naye limodzi patebulo pompano.+

  • Luka 22:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Choncho anayamba kukambirana pakati pawo za amene anakonza chiwembu chimenecho.+

  • Yohane 13:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Atanena zimenezi, Yesu anavutika kwambiri mumtima, ndipo anachitira umboni kuti: “Ndithu ndikukuuzani, mmodzi wa inu andipereka.”+ 22 Ophunzirawo anayamba kuyangʼanizana chifukwa sankadziwa kuti akunena ndani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena