Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 15:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 ndipo inunso mudzandichitira umboni,+ chifukwa mwakhala nane kuchokera pachiyambi.”

  • 1 Petulo 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho, ine monga mkulu mnzanu, amene ndinaona mmene Khristu anavutikira komanso ndikuyembekezera kudzalandira nawo ulemerero umene udzaonekere,+ ndikupempha akulu amene ali pakati panu kuti:

  • 2 Petulo 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Pamene tinkakudziwitsani za mphamvu za Ambuye wathu Yesu Khristu komanso zokhudza kukhalapo* kwake, sitinatengere nkhani zabodza zimene anthu amapeka mochenjera. Koma tinakuuzani zinthu zokhudza ulemerero wake zimene tinachita kuona ndi maso athu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena