Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Musafalitse nkhani yabodza.+ Musamagwirizane ndi munthu woipa pokhala mboni yokonzera wina zoipa.+

  • Ekisodo 23:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Musamagwirizane ndi anthu amene akuneneza munthu mlandu wabodza.* Musamaphe munthu wosalakwa komanso wolungama, chifukwa woipa sindidzamuona kuti ndi wolungama.*+

  • Levitiko 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Musamabe,+ musamapusitse anzanu+ ndiponso musamachitirane chinyengo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena