Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 4:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndipo kudzera mwa ana amene Yehova adzakupatsa kwa mtsikanayu,+ nyumba yako ikhale ngati nyumba ya Perezi,+ amene Tamara anaberekera Yuda.”

  • Rute 4:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mzere wa ana a Perezi+ unayenda chonchi: Perezi anabereka Hezironi,+ 19 Hezironi anabereka Ramu, Ramu anabereka Aminadabu,+

  • 1 Mbiri 2:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tamara,+ mpongozi wake, anamʼberekera Perezi+ ndi Zera. Ana onse a Yuda analipo 5.

      5 Ana a Perezi anali Hezironi ndi Hamuli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena