Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 13:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma mtsogoleri wa sunagoge ataona zimenezi, anakwiya chifukwa Yesu anachiritsa munthu pa Sabata. Choncho anauza gulu la anthu kuti: “Pali masiku 6 amene tikuyenera kugwira ntchito.+ Muzibwera masiku amenewo kudzachiritsidwa, osati tsiku la Sabata.”+

  • Yohane 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno ena mwa Afarisiwo anayamba kunena kuti: “Munthu ameneyu si wochokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata.”+ Ena ankanena kuti: “Kodi munthu wochimwa angachite bwanji zizindikiro ngati zimenezi?”+ Choncho anthuwo anagawanika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena