Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 23:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Tsoka kwa inu alembi ndi Afarisi, anthu achinyengo inu! Chifukwa mumapereka chakhumi cha timbewu ta minti, dilili ndi chitowe,+ koma mumanyalanyaza zinthu zofunika za mʼChilamulo, zomwe ndi chilungamo,+ chifundo+ ndi kukhulupirika. Kupereka zinthu zimenezi nʼkofunika ndithu, koma osanyalanyaza zinthu zinazo.+ 24 Atsogoleri akhungu inu,+ amene mumasefa zakumwa zanu kuti muchotsemo kanyerere+ koma mumameza ngamila.+

  • Yohane 7:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Siyani kuweruza potengera maonekedwe akunja, koma muziweruza ndi chiweruzo cholungama.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena