Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Komanso mfumu inanena kuti, ‘Atamandike Yehova Mulungu wa Isiraeli, amene lero wapereka munthu woti akhale pampando wanga wachifumu, ndipo walola kuti maso anga aone zimenezi.’”

  • Salimo 41:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Atamandike Yehova Mulungu wa Isiraeli,

      Kuyambira panopo mpaka kalekale.*+

      Ame! Ame!

  • Salimo 72:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Atamandike Yehova Mulungu, Mulungu wa Isiraeli,+

      Iye yekha amene amachita zinthu zodabwitsa.+

  • Salimo 106:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Atamandike Yehova, Mulungu wa Isiraeli,

      Mpaka kalekale.*+

      Ndipo anthu onse anene kuti, “Ame!”

      Tamandani Ya,*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena