Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 24:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Koma dziwani izi: Ngati mwininyumba atadziwa nthawi imene wakuba angabwere,+ angakhale maso ndipo sangalole kuti wakubayo athyole nʼkulowa mʼnyumba mwake.+

  • 1 Atesalonika 5:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chifukwa inuyo mukudziwa bwino kuti tsiku la Yehova*+ lidzabwera ndendende ngati wakuba usiku.+

  • 2 Petulo 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Komabe, tsiku la Yehova*+ lidzafika ngati wakuba,+ pamene kumwamba kudzachoka+ ndi mkokomo waukulu. Ndipo zinthu zimene zimapanga kumwamba ndi dziko lapansi zidzatentha kwambiri nʼkusungunuka, moti dziko lapansi ndi ntchito zake zidzaonekera poyera.+

  • Chivumbulutso 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Taona! Ndikubwera ngati wakuba.+ Wosangalala ndi amene akukhalabe maso+ ndiponso amene wavalabe malaya ake akunja, kuti asayende wosavala anthu nʼkuona maliseche ake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena