Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 16:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Koma Yesu anawayankha kuti: “Kunja kukamada mumanena kuti, ‘Nyengo ikhala yabwino, chifukwa kumwamba kwafiira ngati moto.’ 3 Koma mʼmawa mumanena kuti, ‘Lero kukuoneka kuti kugwa mvula, chifukwa kumwamba kwafiira ndipo kuli mitambo.’ Mumadziwa kumasulira kaonekedwe ka kumwamba, koma mukulephera kumasulira zizindikiro za nthawi ino.

  • Luka 19:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Iye anati: “Ngati iwe lero ukanazindikira zinthu zamtendere—* koma tsopano zabisika kuti usathe kuziona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena