Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 34:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Ine ndilipo ndipo ndidzafunafuna nkhosa zanga ndi kuzisamalira.+

  • Ezekieli 34:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Nkhosa imene yasowa ndidzaifunafuna,+ imene yasochera ndidzaibweza. Imene yavulala ndidzaimanga povulalapo ndipo imene ili yofooka ndidzailimbitsa, koma yonenepa ndi yamphamvu ndidzaiwononga. Ndidzaipatsa chiweruzo kuti chikhale chakudya chake.”

  • Mateyu 18:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mukuganiza bwanji? Ngati munthu ali ndi nkhosa 100 ndipo imodzi mwa nkhosazo nʼkusochera,+ kodi sangasiye nkhosa 99 zija mʼphiri nʼkupita kukafunafuna yosocherayo?+ 13 Akaipeza, ndithu ndikukuuzani, amasangalala kwambiri ndi nkhosa imeneyo kusiyana ndi nkhosa 99 zimene sizinasochere zija.

  • Luka 19:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mwana wa munthu anabwera kudzafunafuna ndiponso kudzapulumutsa anthu osochera.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena