-
Machitidwe 6:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Sitefano anali ndi mphamvu ndipo ankachita kuonekeratu kuti Mulungu ali naye. Iye ankachita zinthu zodabwitsa ndi zizindikiro zazikulu pakati pa anthu.
-