Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:29, 30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mpheta ziwiri amazigulitsa kakhobidi kamodzi kochepa mphamvu,* si choncho? Koma palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziwa.+ 30 Ndipotu ngakhale tsitsi lonse lamʼmutu mwanu amaliwerenga.

  • Luka 12:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mpheta 5 amazigulitsa makobidi awiri ochepa mphamvu,* si choncho? Komatu palibe ngakhale imodzi mwa mbalame zimenezi imene Mulungu amaiiwala.*+ 7 Ndipotu ngakhale tsitsi lonse lamʼmutu mwanu amaliwerenga.+ Musachite mantha, ndinu ofunika kwambiri kuposa mpheta zambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena