Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu anamuuza kuti: “Ndithudi ndikukuuza iwe, usiku womwe uno tambala asanalire, undikana katatu.”+

  • Maliko 14:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Atatero Yesu anamuyankha kuti: “Ndithu ndikukuuza iwe kuti lero, usiku womwe uno, tambala asanalire kawiri, undikana katatu.”+

  • Luka 22:61
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 61 Zitatero Ambuye anacheuka nʼkuyangʼana Petulo, ndipo Petulo anakumbukira mawu amene Ambuye anamuuza aja akuti: “Tambala asanalire lero, undikana katatu.”+

  • Yohane 13:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Yesu anayankha kuti: “Kodi udzapereka moyo wako chifukwa cha ine? Ndithudi ndikukuuza iwe, tambala asanalire undikana katatu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena