Yesaya 50:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Msana wanga ndinaupereka kwa anthu amene ankandimenyaNdipo masaya anga ndinawapereka kwa anthu amene ankandizula ndevu. Sindinabise nkhope yanga kuti asaichitire zinthu zochititsa manyazi komanso kuti asailavulire.+ Yesaya 53:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Koma iye anabayidwa+ chifukwa cha zolakwa zathu.+Anaphwanyidwa chifukwa cha zochimwa zathu.+ Analandira chilango kuti ife tikhale pamtendere,+Ndipo chifukwa cha mabala ake ifeyo tinachiritsidwa.+ Mateyu 26:67, 68 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 67 Ndiyeno anayamba kumulavulira kunkhope+ komanso kumumenya nkhonya.+ Ena anamuwomba mbama+ 68 nʼkunena kuti: “Losera tione Khristu iwe. Wakumenya ndi ndani?” Maliko 14:65 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 65 Ndipo ena anayamba kumulavulira,+ kumuphimba nkhope nʼkumamukhoma nkhonya. Iwo ankamuuza kuti: “Losera!” Atamuwomba mbama, asilikali apakhoti anamutenga.+
6 Msana wanga ndinaupereka kwa anthu amene ankandimenyaNdipo masaya anga ndinawapereka kwa anthu amene ankandizula ndevu. Sindinabise nkhope yanga kuti asaichitire zinthu zochititsa manyazi komanso kuti asailavulire.+
5 Koma iye anabayidwa+ chifukwa cha zolakwa zathu.+Anaphwanyidwa chifukwa cha zochimwa zathu.+ Analandira chilango kuti ife tikhale pamtendere,+Ndipo chifukwa cha mabala ake ifeyo tinachiritsidwa.+
67 Ndiyeno anayamba kumulavulira kunkhope+ komanso kumumenya nkhonya.+ Ena anamuwomba mbama+ 68 nʼkunena kuti: “Losera tione Khristu iwe. Wakumenya ndi ndani?”
65 Ndipo ena anayamba kumulavulira,+ kumuphimba nkhope nʼkumamukhoma nkhonya. Iwo ankamuuza kuti: “Losera!” Atamuwomba mbama, asilikali apakhoti anamutenga.+