Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 14:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pa nthawiyo Herode, wolamulira chigawo,* anamva za Yesu+

  • Maliko 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno Mfumu Herode inamva zimenezi chifukwa dzina la Yesu linatchuka kwambiri ndipo anthu ankanena kuti: “Yohane Mʼbatizi wauka kwa akufa nʼchifukwa chake akuchita ntchito zamphamvu.”+

  • Luka 9:7-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Tsopano Herode,* wolamulira chigawo,* anamva zonse zimene zinkachitika. Iye anathedwa nzeru chifukwa ena ankanena kuti Yohane waukitsidwa.+ 8 Koma ena ankanena kuti Eliya waonekera. Enanso ankanena kuti mmodzi wa aneneri akale wauka.+ 9 Ndiyeno Herode anati: “Yohane ndinamudula mutu.+ Nanga amene akuchita zomwe ndikumvazi ndi ndani?” Choncho ankafunitsitsa atamuona.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena