Maliko 15:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Komanso iwo anakakamiza munthu wina amene ankangodutsa dzina lake Simoni wa ku Kurene kuti asenze mtengo wake wozunzikirapo.* Iyeyu ankachokera kudera lakumidzi ndipo anali bambo wa Alekizanda ndi Rufu.+ Yohane 19:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Iye ananyamula yekha mtengo wozunzikirapo* nʼkutuluka kupita kumalo amene ankatchulidwa kuti Chibade,+ koma pa Chiheberi ankatchulidwa kuti Gologota.+
21 Komanso iwo anakakamiza munthu wina amene ankangodutsa dzina lake Simoni wa ku Kurene kuti asenze mtengo wake wozunzikirapo.* Iyeyu ankachokera kudera lakumidzi ndipo anali bambo wa Alekizanda ndi Rufu.+
17 Iye ananyamula yekha mtengo wozunzikirapo* nʼkutuluka kupita kumalo amene ankatchulidwa kuti Chibade,+ koma pa Chiheberi ankatchulidwa kuti Gologota.+