Ekisodo 20:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Muzilemekeza bambo anu ndi mayi anu+ kuti mukhale ndi moyo nthawi yaitali mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.+ Deuteronomo 5:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Muzilemekeza bambo anu ndi mayi anu+ mogwirizana ndi zimene Yehova Mulungu wanu anakulamulani, kuti mukhale ndi moyo nthawi yaitali komanso kuti zinthu zikuyendereni bwino mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.+ Aefeso 6:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ana inu, muzimvera makolo anu+ mogwirizana ndi zimene Ambuye amafuna, chifukwa kuchita zimenezi nʼkoyenera. Akolose 3:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ana inu, muzimvera makolo anu pa zinthu zonse,+ chifukwa zimenezi zimasangalatsa Ambuye.
12 Muzilemekeza bambo anu ndi mayi anu+ kuti mukhale ndi moyo nthawi yaitali mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.+
16 Muzilemekeza bambo anu ndi mayi anu+ mogwirizana ndi zimene Yehova Mulungu wanu anakulamulani, kuti mukhale ndi moyo nthawi yaitali komanso kuti zinthu zikuyendereni bwino mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani.+
6 Ana inu, muzimvera makolo anu+ mogwirizana ndi zimene Ambuye amafuna, chifukwa kuchita zimenezi nʼkoyenera.