Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:9-11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsiku linanso analota maloto ena, ndipo anauza abale akewo kuti: “Leronso ndinalota maloto ena. Ndinalota dzuwa ndi mwezi ndiponso nyenyezi zokwana 11 zikundigwadira.”+ 10 Kenako anafotokozeranso bambo ake ndi abale ake malotowo. Koma bambo ake anamʼdzudzula kuti: “Kodi maloto akowa akutanthauza chiyani? Kodi zoona ineyo ndi mayi akowa, komanso abale akowa tidzagwada pansi pamaso pa iwe?” 11 Abale akewo anamuchitira nsanje,+ koma bambo ake anasunga mawuwo mumtima.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena