Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 42:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anapitiriza kuti: “Ine ndamva kuti ku Iguputo kuli tirigu. Pitani mukatigulire kuti tikhalebe ndi moyo, tisafe ndi njala.”+

  • Genesis 42:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Yosefe ndi amene anali wolamulira mʼdzikomo+ ndipo ndi amene ankagulitsa tirigu kwa anthu onse ochokera kumayiko ena onse.+ Choncho abale a Yosefe anafika kwa iye ndipo anagwada nʼkumuweramira mpaka nkhope zawo pansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena