Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Dziko lonseli lidzakhala bwinja ndipo lidzakhala chinthu chochititsa mantha. Mitundu imeneyi idzatumikira mfumu ya ku Babulo zaka 70.”’+

  • Amosi 5:25-27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Inu amʼnyumba ya Isiraeli,

      Kodi pamene munali mʼchipululu muja kwa zaka 40, munandipatsa nsembe zanyama ndi zopereka zina?+

      26 Koma inu mudzanyamula Sakuti mfumu yanu ndi Kaiwani,*

      Mafano amene munapanga a mulungu wanu wa nyenyezi.

      27 Ndipo ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kwambiri ndi ku Damasiko,’+ watero Mulungu wa magulu ankhondo akumwamba, amene dzina lake ndi Yehova.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena