Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 53:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye anaponderezedwa ndipo anatengedwa popanda kuweruzidwa mwachilungamo.

      Ndi ndani amene anaganizira tsatanetsatane wa mʼbadwo wa makolo ake?*

      Popeza iye anadulidwa mʼdziko la anthu amoyo.+

      Iye anakwapulidwa* chifukwa cha zolakwa za anthu anga.+

  • Machitidwe 3:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mulungu wa Abulahamu, wa Isaki ndi wa Yakobo,+ Mulungu wa makolo athu, ndi amene walemekeza Mtumiki wake+ Yesu,+ amene inu munamupereka+ ndiponso kumukana pamaso pa Pilato, ngakhale kuti Pilatoyo ankafuna kumumasula. 14 Inde, inu munakana woyera ndi wolungamayo, ndipo munapempha kuti akumasulireni munthu wopha anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena