Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Saulo anavomereza zoti Sitefano aphedwe.+

      Tsiku limenelo, mpingo umene unali ku Yerusalemu unayamba kuzunzidwa koopsa. Choncho ophunzira onse, kupatula atumwi okha, anabalalika nʼkupita mʼzigawo za Yudeya ndi Samariya.+

  • Machitidwe 22:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Komanso pamene Sitefano, mboni yanu ankaphedwa, ine ndinali pomwepo ndipo ndinavomereza. Ndi inenso amene ndinkayangʼanira malaya akunja a anthu amene ankamuphawo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena