Salimo 147:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Imbirani amene amaphimba mapiri ndi mitambo,Amene amapereka mvula padziko lapansi,+Amenenso amameretsa udzu+ mʼmapiri. Yeremiya 5:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Mumtima mwawo sanena kuti: “Tiyeni tsopano tiope Yehova Mulungu wathu,Amene amatigwetsera mvula mʼnyengo yake,Amatigwetsera mvula yoyamba ndi yomalizira,Amene amaonetsetsa kuti tikukolola pa nthawi yake.”*+ Mateyu 5:45 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 45 kuti musonyeze kuti ndinudi ana a Atate wanu wakumwamba.+ Chifukwa iye amawalitsira dzuwa lake anthu abwino ndi oipa omwe, ndipo amagwetsera mvula anthu olungama ndi osalungama omwe.+
8 Imbirani amene amaphimba mapiri ndi mitambo,Amene amapereka mvula padziko lapansi,+Amenenso amameretsa udzu+ mʼmapiri.
24 Mumtima mwawo sanena kuti: “Tiyeni tsopano tiope Yehova Mulungu wathu,Amene amatigwetsera mvula mʼnyengo yake,Amatigwetsera mvula yoyamba ndi yomalizira,Amene amaonetsetsa kuti tikukolola pa nthawi yake.”*+
45 kuti musonyeze kuti ndinudi ana a Atate wanu wakumwamba.+ Chifukwa iye amawalitsira dzuwa lake anthu abwino ndi oipa omwe, ndipo amagwetsera mvula anthu olungama ndi osalungama omwe.+