-
Machitidwe 14:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Paulo ndi Baranaba ali ku Ikoniyo, analowa mʼsunagoge wa Ayuda ndipo analankhula bwino kwambiri moti Ayuda ambiri limodzi ndi Agiriki anakhala okhulupirira.
-