Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 110:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 110 Yehova anauza Ambuye wanga kuti:

      “Khala kudzanja langa lamanja+

      Mpaka nditaika adani ako kuti akhale chopondapo mapazi ako.”+

  • Luka 20:42, 43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Chifukwa Davideyo ananena mʼbuku la Masalimo kuti, ‘Yehova* anauza Ambuye wanga kuti: “Khala kudzanja langa lamanja 43 mpaka nditaika adani ako kuti akhale chopondapo mapazi ako.”’+

  • 1 Akorinto 15:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Chifukwa ayenera kukhala mfumu nʼkumalamulira mpaka Mulungu ataika adani onse pansi pa mapazi ake.+

  • Aheberi 10:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma munthu ameneyu anapereka nsembe imodzi yamachimo yothandiza mpaka kalekale, ndipo anakhala kudzanja lamanja la Mulungu.+ 13 Kuyambira nthawi imeneyo, akudikira mpaka pamene adani ake adzaikidwe kuti akhale chopondapo mapazi ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena