Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Timoteyo 4:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Komabe mawu ouziridwa amanena momveka bwino kuti nthawi ina mʼtsogolo, chikhulupiriro cha anthu ena chidzatha chifukwa chomvetsera mawu ouziridwa omwe ndi osocheretsa,+ ndiponso zinthu zimene ziwanda zimaphunzitsa.

  • 2 Timoteyo 4:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chifukwa idzafika nthawi imene anthu sadzafunanso kuphunzitsidwa zolondola,+ koma mogwirizana ndi zimene amalakalaka, adzapeza aphunzitsi oti aziwauza zowakomera mʼkhutu.+ 4 Iwo adzasiya kumvetsera choonadi nʼkumamvetsera nkhani zonama.

  • 1 Yohane 2:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ana inu, ino ndi nthawi yakumapeto. Munamva kuti wokana Khristu akubwera,+ ndipo panopa okana Khristu ambiri aonekera.+ Chifukwa cha zimenezi tikudziwa kuti ino ndi nthawi yakumapeto. 19 Amenewo anachoka pakati pathu, koma sanali mʼgulu lathu,*+ chifukwa akanakhala a mʼgulu lathu, akanakhalabe ndi ife. Koma anachoka kuti zidziwike kuti si onse amene ali mʼgulu lathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena