Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 5:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yesu anamuuza kuti: “Nyamuka, nyamula machira akowa nʼkuyamba kuyenda.”+ 9 Nthawi yomweyo munthu uja anachira ndipo ananyamula machira akewo nʼkuyamba kuyenda.

      Limeneli linali tsiku la Sabata.

  • Machitidwe 9:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndiyeno Petulo anamuuza kuti: “Eneya, Yesu Khristu akukuchiritsa.+ Dzuka ndipo ukonze pabedi lakolo.”+ Nthawi yomweyo anadzuka.

  • Machitidwe 14:8-10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ku Lusitara, kunali munthu wina wolumala miyendo ndipo anali atakhala pansi. Iyeyu anabadwa wolumala ndipo anali asanayendepo. 9 Munthu ameneyu ankamvetsera pamene Paulo ankalankhula. Ndiyeno Paulo atamuyangʼanitsitsa anaona kuti ali ndi chikhulupiriro choti angachiritsidwe.+ 10 Choncho Paulo analankhula mokweza mawu kuti: “Imirira!” Atatero, wolumalayo anadumpha nʼkuyamba kuyenda.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena