Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Abulamu ali ndi zaka 99, Yehova anaonekera kwa iye nʼkumuuza kuti: “Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse. Uziyenda mʼnjira zanga ndipo ukhale wopanda cholakwa. 2 Ndidzakhazikitsa pangano langa pakati pa ine ndi iwe+ ndipo ndidzachulukitsa kwambiri mbadwa zako.”+

  • Genesis 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Muzichita mdulidwe* kuti ukhale chizindikiro cha pangano la pakati pa ine ndi inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena