Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 3:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Amene amakhulupirira Mwanayo adzalandira moyo wosatha.+ Wosamvera Mwanayo sadzalandira moyowu,+ koma mkwiyo wa Mulungu udzakhalabe pa iye.+

  • Aroma 3:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma tsopano, zadziwika kuti munthu akhoza kukhala wolungama kwa Mulungu popanda kutsatira Chilamulo.+ Zimenezi zinatchulidwanso mʼChilamulo komanso zimene aneneri analemba.+ 22 Kuonedwa wolungama ndi Mulungu kumeneku kungatheke kwa onse amene amasonyeza kuti amakhulupirira Yesu Khristu, chifukwa palibe kusiyana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena