Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mulungu anatiululira ifeyo zinthu zimenezi+ kudzera mwa mzimu wake,+ chifukwa mzimu umafufuza zinthu zonse, ngakhale zinthu zozama za Mulungu.+

  • 1 Akorinto 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ife sitinalandire mzimu wa dziko, koma mzimu wochokera kwa Mulungu,+ kuti tidziwe zinthu zimene Mulungu watipatsa mokoma mtima.

  • 2 Akorinto 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iye watidinda chidindo chake.+ Chidindo chimenechi ndi mzimu woyera+ womwe uli mʼmitima mwathu ndipo uli ngati madalitso amʼtsogolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena