Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Atesalonika 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Usiku ndi masana timapemphera mopembedzera kuchokera pansi pamtima kuti tidzakuoneni pamasomʼpamaso* nʼkukupatsani zimene zikufunika kuti chikhulupiriro chanu chikhale cholimba.+

  • 2 Timoteyo 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndikuthokoza Mulungu amene ndikumuchitira utumiki wopatulika ngati mmene makolo anga akale anachitira. Ndikuuchita ndi chikumbumtima choyera ndipo sindiiwala kukutchula mʼmapemphero anga opembedzera, usana ndi usiku.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena