Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Agalatiya 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma ataona kuti ndapatsidwa ntchito yolalikira uthenga wabwino kwa anthu osadulidwa,+ mofanana ndi Petulo amene anapatsidwa ntchito yoti akalalikire uthenga wabwino kwa anthu odulidwa,

  • Aefeso 3:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho, ine Paulo, ndili mʼndende+ chifukwa ndili kumbali ya Khristu Yesu komanso chifukwa chothandiza inu, anthu a mitundu ina— 2 ndithudi, munamva kuti ndinalandira udindo wokuthandizani+ kuti mupindule ndi kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu,

  • Akolose 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndinakhala mtumiki wa mpingo umenewu mogwirizana ndi udindo+ umene Mulungu anandipatsa woti ndilalikire mawu a Mulungu mokwanira, kuti inuyo mupindule.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena