Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoweli 2:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Zimenezi zikadzachitika ndidzapereka* mzimu wanga+ kwa chamoyo chilichonse,

      Ndipo ana anu aamuna ndi ana anu aakazi adzalosera.

      Amuna achikulire adzalota maloto,

      Ndipo anyamata adzaona masomphenya.+

  • Machitidwe 21:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsiku lotsatira tinanyamuka nʼkukafika ku Kaisareya ndipo tinapita kunyumba kwa mlaliki wina dzina lake Filipo. Iyeyu anali mmodzi wa amuna 7+ a mbiri yabwino aja, ndipo tinakhala naye. 9 Filipo anali ndi ana aakazi 4 osakwatiwa,* amene ankanenera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena