Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Akorinto 3:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Sitinganene kuti ndife oyenera kugwira ntchito imeneyi chifukwa cha mphamvu zathu, koma ndife oyenera kugwira ntchitoyi chifukwa cha Mulungu,+ 6 ndipo iyeyo anationa kuti ndife oyenera kukhala atumiki a pangano latsopano,+ osati kudzera mʼmalamulo olembedwa,+ koma kudzera mu mzimu. Malamulo olembedwa amaweruza munthu kuti afe,+ koma mzimu umapatsa munthu moyo.+

  • Akolose 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma mukuyenera kupitiriza kukhala mogwirizana ndi chikhulupiriro chanu,+ muli okhazikika pamaziko,+ muli olimba+ komanso muli osasunthika pa chiyembekezo cha uthenga wabwino umene munamva, umenenso unalalikidwa padziko lonse.*+ Ineyo Paulo ndinakhala mtumiki wa uthenga wabwino umenewu.+

  • 1 Timoteyo 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndikuthokoza Khristu Yesu Ambuye wathu, amene anandipatsa mphamvu nʼkundipatsanso utumiki chifukwa anaona kuti ndine wokhulupirika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena