Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 12:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho Petulo anatsekeredwa mʼndendemo, koma mpingo unkamupempherera kwambiri kwa Mulungu.+

  • Aroma 15:30-32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Choncho abale, ndikukupemphani kudzera mwa Ambuye wathu Yesu Khristu komanso chikondi cha mzimu, kuti muzilimbikira kundipempherera kwa Mulungu ndipo nanenso ndikulimbikira kupemphera.+ 31 Tilimbikire kupemphera kuti ndikapulumutsidwe+ kwa anthu osakhulupirira a ku Yudeya ndiponso kuti oyera a ku Yerusalemu akalandire bwino mphatso imene ndatenga.+ 32 Ngati Mulungu angalole, ndidzabwera kwa inu mosangalala ndipo tidzalimbikitsana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena