Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 16:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Chifukwa Mwana wa munthu adzabwera mu ulemerero wa Atate wake limodzi ndi angelo ake. Pa nthawi imeneyo adzapereka mphoto kwa aliyense mogwirizana ndi makhalidwe ake.+

  • Afilipi 3:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chifukwa pali anthu ambiri amene akuchita zinthu ngati adani a mtengo wozunzikirapo* wa Khristu. Kale ndinkawatchula pafupipafupi koma pano ndimawatchula ndikugwetsa misozi. 19 Anthu amenewo akuyembekezera kuwonongedwa ndipo mulungu wawo ndi mimba zawo. Iwo amanyadira zinthu zimene akuyenera kuchita nazo manyazi ndipo amangoganizira zinthu zapadziko lapansi.+

  • 2 Timoteyo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Alekizanda wosula zinthu zakopa uja, anandichitira zoipa kwambiri. Yehova* adzamubwezera mogwirizana ndi ntchito zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena