-
Yuda 4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Ndatero chifukwa chakuti anthu ena alowa mozemba pakati panu. Malemba anasonyezeratu kalekale kuti anthu amenewa adzaweruzidwa. Anthuwa ndi osaopa Mulungu ndipo atenga kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu wathu kukhala chifukwa chochitira khalidwe lopanda manyazi.*+ Komanso asonyeza kuti ndi osakhulupirika kwa Ambuye wathu mmodzi yekha amene anatigula, Yesu Khristu.+
-