Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 16:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pa tsiku limenelo simudzandifunsanso mafunso. Ndithudi ndikukuuzani, ngati mungapemphe chilichonse kwa Atate+ mʼdzina langa adzakupatsani.+

  • Aroma 12:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kondwerani chifukwa cha chiyembekezo. Muzipirira mavuto.+ Muzilimbikira kupemphera.+

  • 1 Petulo 5:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho dzichepetseni pamaso pa Mulungu wathu wamphamvu* kuti adzakukwezeni nthawi yake ikadzakwana.+ 7 Muzichita zimenezi pamene mukumutulira nkhawa zanu zonse,+ chifukwa amakufunirani zabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena