Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 4:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho ine, amene ndili mʼndende+ chifukwa cha Ambuye, ndikukuchondererani kuti muzichita zinthu mogwirizana+ ndi kuitana kumene anakuitanani. 2 Nthawi zonse muzichita zinthu modzichepetsa,*+ mofatsa, moleza mtima+ ndiponso muzilolerana chifukwa cha chikondi.+

  • 1 Atesalonika 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Komanso tikukulimbikitsani abale, kuti muzichenjeza* anthu ochita zosalongosoka,+ muzilankhula molimbikitsa kwa anthu amene ali ndi nkhawa,* muzithandiza ofooka, muzikhala oleza mtima kwa onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena