Machitidwe 18:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Sila+ ndi Timoteyo+ atafika kuchokera ku Makedoniya, Paulo anatanganidwa kwambiri ndi ntchito yolalikira mawu a Mulungu. Iye ankachitira umboni kwa Ayuda ndiponso kuwatsimikizira kuti Yesu ndiyedi Khristu.+
5 Sila+ ndi Timoteyo+ atafika kuchokera ku Makedoniya, Paulo anatanganidwa kwambiri ndi ntchito yolalikira mawu a Mulungu. Iye ankachitira umboni kwa Ayuda ndiponso kuwatsimikizira kuti Yesu ndiyedi Khristu.+