1 Timoteyo 4:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma uzipewa nkhani zonama zosalemekeza Mulungu+ ngati zimene amayi ena okalamba amakamba. Mʼmalomwake, uzidziphunzitsa nʼcholinga choti ukhalebe wodzipereka kwa Mulungu. 2 Timoteyo 4:3, 4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Chifukwa idzafika nthawi imene anthu sadzafunanso kuphunzitsidwa zolondola,+ koma mogwirizana ndi zimene amalakalaka, adzapeza aphunzitsi oti aziwauza zowakomera mʼkhutu.+ 4 Iwo adzasiya kumvetsera choonadi nʼkumamvetsera nkhani zonama. Tito 1:13, 14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Umboni umenewu ndi woona. Chifukwa cha zimenezi, pitiriza kuwadzudzula mwamphamvu kuti akhale ndi chikhulupiriro cholimba. 14 Asamamvetsere nthano zachiyuda ndiponso kutsatira malamulo a anthu amene asiya choonadi.
7 Koma uzipewa nkhani zonama zosalemekeza Mulungu+ ngati zimene amayi ena okalamba amakamba. Mʼmalomwake, uzidziphunzitsa nʼcholinga choti ukhalebe wodzipereka kwa Mulungu.
3 Chifukwa idzafika nthawi imene anthu sadzafunanso kuphunzitsidwa zolondola,+ koma mogwirizana ndi zimene amalakalaka, adzapeza aphunzitsi oti aziwauza zowakomera mʼkhutu.+ 4 Iwo adzasiya kumvetsera choonadi nʼkumamvetsera nkhani zonama.
13 Umboni umenewu ndi woona. Chifukwa cha zimenezi, pitiriza kuwadzudzula mwamphamvu kuti akhale ndi chikhulupiriro cholimba. 14 Asamamvetsere nthano zachiyuda ndiponso kutsatira malamulo a anthu amene asiya choonadi.