Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yudasi atalandira mkatewo, Satana analowa mwa iye.+ Choncho Yesu anamuuza kuti: “Zimene wakonza kuti uchite, zichite mwamsanga.”

  • Machitidwe 5:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Petulo anati: “Hananiya, nʼchifukwa chiyani Satana wakulimbitsa mtima kuti unamize+ mzimu woyera+ nʼkubisa ndalama zina za mundawo?

  • 1 Timoteyo 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ena mwa anthuwa ndi Hemenayo+ ndi Alekizanda, ndipo ndawapereka kwa Satana+ kuti akalangidwa, aphunzirepo kanthu nʼkusiya kunyoza Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena