Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Timoteyo 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kapolo wa Ambuye sayenera kukangana ndi anthu. Koma ayenera kukhala wodekha kwa onse,+ woyenerera kuphunzitsa, wougwira mtima ena akamulakwira+

  • Yakobo 3:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kodi pakati panu pali aliyense wanzeru ndi womvetsa zinthu? Ngati alipo asonyeze zimenezi pochita zinthu zabwino pa moyo wake. Azichita zinthu zonse mofatsa, lomwe ndi khalidwe limene limabwera chifukwa cha nzeru.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena