Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 ndidzakupatsaninso mvula pa nthawi yake mʼdziko lanu, mvula yoyambirira ndi mvula yomaliza, ndipo mudzakolola mbewu zanu nʼkukhala ndi vinyo watsopano komanso mafuta.+

  • Yeremiya 5:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mumtima mwawo sanena kuti:

      “Tiyeni tsopano tiope Yehova Mulungu wathu,

      Amene amatigwetsera mvula mʼnyengo yake,

      Amatigwetsera mvula yoyamba ndi yomalizira,

      Amene amaonetsetsa kuti tikukolola pa nthawi yake.”*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena