Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 22:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kenako iwo anafika pamalo amene Mulungu woona anamuuza Abulahamu. Atafika pamalowo, iye anamanga guwa lansembe nʼkuyala nkhuni zija paguwapo. Atatero, anamanga Isaki mwana wakeyo manja ndi miyendo nʼkumugoneka paguwapo, pamwamba pa nkhuni.+

  • Genesis 22:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno mngeloyo anati: “Usamuvulaze mwanayo ndipo usamuchite chilichonse. Tsopano ndadziwa kuti umaopa Mulungu, chifukwa sunakane kupereka kwa ine mwana wako mmodzi yekhayo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena