Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Yehova adzakupangani kukhala anthu ake oyera,+ mogwirizana ndi zimene analumbira kwa inu,+ chifukwa mukupitiriza kusunga malamulo a Yehova Mulungu wanu ndipo mukuyenda mʼnjira zake.

  • Aroma 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho abale, ndikukudandaulirani mwa chifundo chachikulu cha Mulungu kuti mupereke matupi anu+ ngati nsembe yamoyo, yoyera+ ndiponso yovomerezeka kwa Mulungu, yomwe ndi utumiki wopatulika pogwiritsa ntchito luso la kuganiza.+

  • Aheberi 12:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Muziyesetsa kukhala mwamtendere ndi anthu onse,+ komanso kukhala oyera+ chifukwa ngati munthu si woyera, sadzaona Ambuye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena