Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 15:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma aliyense pa nthawi yoyenera: Choyamba Khristu, amene ndi chipatso choyambirira,+ kenako anthu a Khristu pa nthawi ya kukhalapo* kwake.+

  • 1 Akorinto 15:52
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 mʼkanthawi kochepa, mʼkuphethira kwa diso, pa kulira kwa lipenga lomaliza. Chifukwa lipenga lidzalira,+ kenako akufa adzaukitsidwa ndi matupi oti sangawonongeke ndipo tidzasintha.

  • Afilipi 3:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Cholinga changa nʼchoti ndimudziwe komanso kuti ndidziwe mphamvu za amene anamuukitsa kwa akufa.+ Ndikufunanso kuti ndivutike ngati mmene iye anavutikira,+ mpaka kulolera kufa ngati mmene iye anafera.+ 11 Ndachita zimenezi kuti ngati nʼkotheka ndidzapeze mwayi wodzauka kwa akufa pa kuuka koyamba.+

  • 1 Atesalonika 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Chifukwa Ambuyewo adzatsika kuchoka kumwamba ndi mfuu yolamula. Mawu awo adzamveka kuti ndi a mkulu wa angelo+ ndipo adzanyamula lipenga la Mulungu mʼdzanja lawo. Ndipo amene anafa mwa Khristu adzakhala oyambirira kuuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena