Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 8
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Zimene Zili Mʼbuku la Deuteronomo

      • Anawauzanso madalitso amene Yehova adzawapatse (1-9)

        • “Munthu sakhala ndi moyo ndi chakudya chokha” (3)

      • Musaiwale Yehova (10-20)

Deuteronomo 8:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 3:1, 2
  • +Ge 15:18

Deuteronomo 8:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 2:7
  • +Eks 16:4; 20:20
  • +De 13:3; Miy 17:3

Deuteronomo 8:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 16:3
  • +Eks 16:31; Sl 78:24
  • +Mt 4:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/1/2004, ptsa. 13-14

    8/15/1999, ptsa. 25-26

    5/1/1994, tsa. 3

Deuteronomo 8:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 29:5; Ne 9:21

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/15/2004, tsa. 26

Deuteronomo 8:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 3:12; 1Ak 11:32; Ahe 12:5-7; Chv 3:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/1994, tsa. 3

Deuteronomo 8:7

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti, “makhwawa a madzi.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:8; Le 26:4; De 11:11, 12

Deuteronomo 8:8

Mawu a M'munsi

  • *

    “Makangaza” ndi mtundu wa chipatso. Ena amati chimanga chachizungu.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 13:23
  • +Eze 20:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2011, ptsa. 11-13

    6/15/2006, ptsa. 16-17

    5/15/2000, ptsa. 25, 27

Deuteronomo 8:9

Mawu a M'munsi

  • *

    Kapena kuti, “mkuwa.”

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/1/2013, ptsa. 12-13

Deuteronomo 8:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:10-12

Deuteronomo 8:11

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/1/2006, tsa. 28

    Sukulu ya Utumiki, tsa. 20

Deuteronomo 8:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ho 13:6

Deuteronomo 8:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 9:4; 32:15
  • +Sl 106:21

Deuteronomo 8:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 1:19; Yer 2:6
  • +Nu 20:11

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/1992, tsa. 24

Deuteronomo 8:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 16:35
  • +De 8:2
  • +Ahe 12:11

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/1999, tsa. 25

Deuteronomo 8:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ho 12:8

Deuteronomo 8:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 127:1; Ho 2:8
  • +De 7:12

Deuteronomo 8:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:25, 26; 30:17, 18; Yos 23:12, 13

Deuteronomo 8:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Da 9:11, 12

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 8:1Miy 3:1, 2
Deut. 8:1Ge 15:18
Deut. 8:2De 2:7
Deut. 8:2Eks 16:4; 20:20
Deut. 8:2De 13:3; Miy 17:3
Deut. 8:3Eks 16:3
Deut. 8:3Eks 16:31; Sl 78:24
Deut. 8:3Mt 4:4
Deut. 8:4De 29:5; Ne 9:21
Deut. 8:5Miy 3:12; 1Ak 11:32; Ahe 12:5-7; Chv 3:19
Deut. 8:7Eks 3:8; Le 26:4; De 11:11, 12
Deut. 8:8Nu 13:23
Deut. 8:8Eze 20:6
Deut. 8:10De 6:10-12
Deut. 8:12Ho 13:6
Deut. 8:14De 9:4; 32:15
Deut. 8:14Sl 106:21
Deut. 8:15De 1:19; Yer 2:6
Deut. 8:15Nu 20:11
Deut. 8:16Eks 16:35
Deut. 8:16De 8:2
Deut. 8:16Ahe 12:11
Deut. 8:17Ho 12:8
Deut. 8:18Sl 127:1; Ho 2:8
Deut. 8:18De 7:12
Deut. 8:19De 4:25, 26; 30:17, 18; Yos 23:12, 13
Deut. 8:20Da 9:11, 12
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 8:1-20

Deuteronomo

8 “Muonetsetse kuti mukusunga lamulo lililonse limene ndikukupatsani lero, kuti mupitirize kukhala ndi moyo+ komanso kuti muchuluke, nʼkupita kukatenga dziko limene Yehova analumbira kwa makolo anu.+ 2 Muzikumbukira njira yaitali imene Yehova Mulungu wanu anakuyendetsani mʼchipululu zaka 40 zonsezi.+ Iye anakuyendetsani mʼchipululu kuti akuphunzitseni kudzichepetsa komanso kukuyesani+ pofuna kudziwa zimene zinali mumtima mwanu,+ kuti aone ngati mungasunge malamulo ake kapena ayi. 3 Anakuphunzitsani kudzichepetsa pokulolani kuti mukhale ndi njala+ nʼkukudyetsani mana,+ amene inu kapena makolo anu sankawadziwa. Anachita zimenezi kuti mudziwe kuti munthu sangakhale ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu alionse ochokera mʼkamwa mwa Yehova.+ 4 Zovala zimene munavala sizinathe ndipo mapazi anu sanatupe pa zaka 40 zimenezi.+ 5 Inu mukudziwa bwino mumtima mwanu kuti Yehova Mulungu wanu ankakulangizani, ngati mmene bambo amalangizira mwana wake.+

6 Tsopano muzisunga malamulo a Yehova Mulungu wanu poyenda mʼnjira zake ndi kumuopa. 7 Chifukwa Yehova Mulungu wanu akukulowetsani mʼdziko labwino,+ dziko la mitsinje ya madzi,* akasupe ndi madzi ochuluka amene akuyenda mʼzigwa ndi mʼdera lamapiri, 8 dziko la tirigu, balere, mphesa, mitengo ya mkuyu ndi makangaza,*+ dziko la maolivi opangira mafuta ndiponso la uchi,+ 9 mʼdziko limene simudzasowa chakudya komanso simudzasowa chilichonse, dziko limene miyala yake amapangira zitsulo, limenenso mʼmapiri ake mudzakumbamo kopa.*

10 Mukadzadya nʼkukhuta, mudzatamande Yehova Mulungu wanu chifukwa cha dziko labwino limene wakupatsani.+ 11 Samalani kuti musaiwale Yehova Mulungu wanu polephera kusunga malamulo, zigamulo ndi malangizo ake amene ndikukupatsani lero. 12 Mukadzadya nʼkukhuta, kumanga nyumba zabwino nʼkukhalamo,+ 13 ngʼombe zanu ndi nkhosa zanu nʼkuchuluka, siliva ndi golide wanu nʼkuwonjezeka ndiponso nʼkukhala ndi zinthu zochuluka, 14 musakalole kuti mtima wanu ukayambe kunyada+ nʼkukuchititsani kuiwala Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo, mʼnyumba yaukapolo,+ 15 amene anakuyendetsani mʼchipululu chachikulu ndi chochititsa mantha,+ chokhala ndi njoka zapoizoni, zinkhanira ndiponso nthaka youma yopanda madzi. Iye anachititsa kuti madzi atuluke pamwala wolimba,+ 16 anakudyetsani mana+ mʼchipululu, chakudya chimene makolo anu sankachidziwa, kuti akuphunzitseni kudzichepetsa+ komanso kukuyesani kuti mʼtsogolo zinthu zidzakuyendereni bwino.+ 17 Ngati mumtima mwanu munganene kuti, ‘Chuma ichi ndachipeza chifukwa cha ntchito ya manja anga komanso mphamvu zanga,’+ 18 muzikumbukira kuti ndi Yehova Mulungu wanu amene amakupatsani mphamvu kuti mupeze chuma,+ pofuna kusunga pangano lake limene analumbira kwa makolo anu, ngati mmene zilili lero.+

19 Koma mukadzaiwala Yehova Mulungu wanu nʼkutsatira milungu ina, kuitumikira ndiponso kuigwadira, ndikukuchenjezani lero kuti anthu inu mudzatha ndithu.+ 20 Mudzatheratu mofanana ndi mitundu imene Yehova akuiwononga pamaso panu, chifukwa simunamvere mawu a Yehova Mulungu wanu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena